-
Yeremiya 49:2Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
2 “‘Choncho taonani! Masiku akubwera,’ akutero Yehova,
‘Amene ndidzachititsa kuti ku Raba,+ umene ndi mzinda wa Aamoni,+ kumveke chizindikiro chakuti kukubwera nkhondo.*
Mzindawu udzasanduka bwinja ndi mulu wadothi.
Midzi yake yozungulira idzawotchedwa ndi moto.’
‘Ndipo Isiraeli adzatenga dziko la anthu amene analanda dziko lake,’+ akutero Yehova.
-