Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezara 3:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Pofika mwezi wa 7,+ Aisiraeli omwe ankakhala mʼmizinda yawo anasonkhana limodzi mogwirizana ku Yerusalemu.

  • Ezara 9:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Koma kwa nthawi yochepa, Yehova Mulungu wathu watikomera mtima polola anthu ena kuti apulumuke ndipo watipatsa malo otetezeka* mʼmalo ake oyera+ kuti maso athu awale. Mulungu wathu watitsitsimula pangʼono mu ukapolo wathu.

  • Yeremiya 30:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Koma iwe Yakobo mtumiki wanga usachite mantha,” akutero Yehova,

      “Ndipo iwe Isiraeli usaope.+

      Chifukwa ndidzakupulumutsa kuchokera kutali

      Ndidzapulumutsanso ana ako kuchokera kudziko limene anatengedwa kukakhala akapolo.+

      Yakobo adzabwerera ndipo adzakhala mosatekeseka komanso mopanda zosokoneza.

      Sipadzakhala wowaopseza.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena