Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 31:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Koma Aiguputowo ndi anthu wamba ndipo si Mulungu.

      Mahatchi awo ndi zinyama, osati mzimu.+

      Yehova akadzatambasula dzanja lake,

      Aliyense amene amapereka thandizo adzapunthwa

      Ndipo aliyense amene akuthandizidwa adzagwa.

      Onsewo adzawonongedwa nthawi imodzi.

  • Yeremiya 2:36
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 36 Nʼchifukwa chiyani ukuona mopepuka kusakhulupirika kwako?

      Udzachitanso manyazi ndi Iguputo,+

      Ngati mmene unachitira manyazi ndi Asuri.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena