Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yeremiya 23:16, 17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Yehova wa magulu ankhondo akumwamba wanena kuti:

      “Musamvere mawu a aneneri amene akulosera kwa inu.+

      Iwo akungokupusitsani.*

      Iwo akulankhula masomphenya amumtima mwawo,+

      Osati ochokera mʼkamwa mwa Yehova.+

      17 Mobwerezabwereza iwo akuuza anthu amene sakundilemekeza kuti,

      ‘Yehova wanena kuti: “Inu mudzakhala pa mtendere.”’+

      Ndipo aliyense amene amatsatira mtima wake woipawo akumuuza kuti,

      ‘Tsoka silidzakugwerani.’+

  • Ezekieli 13:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Kodi masomphenya amene mwaonawa si abodza ndipo zimene mwaloserazi si zonama pamene mukunena kuti, ‘Yehova wanena kuti,’ pamene ine sindinanene chilichonse?”’

  • Mika 2:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Munthu akatsatira zinthu zopanda pake ndi zachinyengo nʼkunena bodza lakuti:

      “Ndidzakulalikirani zokhudza vinyo ndi chakumwa choledzeretsa,”

      Adzangokhala mlaliki wa anthu awa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena