Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 36:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Pajatu Mulungu ali ndi mphamvu zapamwamba.

      Kodi pali mphunzitsi winanso wofanana naye?

  • Salimo 32:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Inu munati: “Ndidzakupatsa nzeru komanso kukulangiza njira yoti uyendemo.+

      Ndidzakupatsa malangizo ndi kukuyangʼanira.+

  • Salimo 71:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Inu Mulungu, mwandiphunzitsa kuyambira ndili mnyamata,+

      Ndipo mpaka pano ndikupitiriza kulengeza ntchito zanu zodabwitsa.+

  • Salimo 119:102
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 102 Sindinasiye kutsatira zigamulo zanu,

      Chifukwa inu mwandilangiza.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena