Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 32:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Kenako iye analandira golideyo kuchokera kwa anthuwo ndipo pogwiritsa ntchito chosemera, anapanga fano* la mwana wa ngʼombe.+ Zitatero iwo anayamba kunena kuti: “Uyu ndi Mulungu wanu, Aisiraeli inu, amene anakutulutsani mʼdziko la Iguputo.”+

  • Deuteronomo 7:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Koma inu mudzawachitire zotsatirazi: Mudzagwetse maguwa awo ansembe komanso kuphwanya zipilala zawo zopatulika.+ Mudzadule mizati yawo yopatulika+ ndi kuwotcha zifaniziro zawo zogoba.+

  • Deuteronomo 7:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Mudzawotche pamoto zifaniziro zogoba za milungu yawo.+ Musadzalakelake siliva ndi golide wawo kapena kutenga zinthu zimenezi kuti zikhale zanu,+ kuopera kuti zingakutchereni msampha, chifukwa zinthu zimenezi ndi zonyansa kwa Yehova Mulungu wanu.+

  • Oweruza 17:3, 4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Choncho anabweza ndalama zasiliva zokwana 1,100 zija kwa mayi ake. Koma mayi akewo anati: “Ndalamazi ndizipereka kwa Yehova kuti zikhale zopatulika. Ndikufuna kuti iweyo ugwiritse ntchito ndalamazi kukapangitsa chifaniziro chosema ndiponso chifaniziro chachitsulo.+ Choncho ndikukupatsa ndalamazi.”

      4 Mika atabweza ndalamazo kwa mayi ake, mayi akewo anatenga ndalama zasiliva 200 nʼkuzipereka kwa wosula siliva. Wosula silivayo anapanga zifaniziro ziwiri. Zifanizirozi anaziika mʼnyumba ya Mika.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena