Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 10:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Choncho Yehova wa magulu ankhondo akumwamba, Ambuye Wamkulu Koposa, wanena kuti: “Anthu anga amene mukukhala mʼZiyoni, musachite mantha chifukwa cha Msuri amene ankakukwapulani ndi chikwapu+ ndiponso kukumenyani ndi ndodo, ngati mmene ankachitira Iguputo.+

  • Yesaya 10:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Yehova wa magulu ankhondo akumwamba adzamʼkwapula ndi chikwapu+ ngati mmene anachitira pamene anagonjetsa Midiyani pathanthwe la Orebi.+ Adzatambasula ndodo yake ndi kuloza panyanja ndipo adzaikweza mʼmwamba ngati mmene anachitira ndi Iguputo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena