Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezekieli 18:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Iye amapewa kupondereza munthu wosauka, sakongoza zinthu mwa katapira ndipo sauza anthu kuti apereke chiwongoladzanja. Amatsatira zigamulo zanga komanso kuyenda motsatira malamulo anga. Munthu wotere sadzafa chifukwa cha zolakwa za bambo ake. Iye adzapitiriza kukhala ndi moyo ndithu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena