4 Ndi ndani amene anakwerapo kumwamba kenako nʼkutsika?+
Ndi ndani amene anasonkhanitsapo mphepo mʼmanja mwake?
Ndi ndani amene anamangapo madzi pachovala chake?+
Ndi ndani amene anaika malire a dziko lapansi?+
Dzina lake ndi ndani, nanga mwana wake dzina lake ndi ndani? Ndiuzeni ngati mukudziwa.