Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Hoseya 11:8, 9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Kodi ndikusiye chifukwa chiyani iwe Efuraimu?+

      Kodi ndikupereke kwa adani chifukwa chiyani iwe Isiraeli?

      Kodi ndikuchitire zinthu ngati Adima chifukwa chiyani?

      Kodi ndikusinthirenji kukhala ngati Zeboyimu?+

      Koma ndasintha maganizo

      Ndipo ndayamba kukumvera chisoni.+

       9 Sindidzasonyeza mkwiyo wanga woyaka moto.

      Sindidzawononganso Efuraimu+

      Chifukwa ndine Mulungu, osati munthu.

      Ndine Woyera pakati panu,

      Ndipo sindidzabwera kwa inu nditakwiya.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena