Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yeremiya 25:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Choncho ndinatenga kapu imene inali mʼdzanja la Yehova ndipo ndinamwetsa mitundu yonse imene Yehova ananditumizako. Mitunduyo ndi iyi:+

  • Yeremiya 25:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Kenako ndinamwetsanso Farao mfumu ya Iguputo, atumiki ake, akalonga ake ndi anthu ake onse+

  • Yeremiya 46:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Yehova anauza mneneri Yeremiya zokhudza kubwera kwa Nebukadinezara* mfumu ya Babulo kudzaukira dziko la Iguputo. Iye anati:+

  • Ezekieli 29:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Choncho Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, wanena kuti, ‘Ine ndikupereka dziko la Iguputo kwa Nebukadinezara* mfumu ya Babulo.+ Iye adzatenga chuma cha dzikolo komanso kulanda zinthu zake zochuluka. Zimenezi zidzakhala malipiro a asilikali ake.

  • Ezekieli 30:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Lupanga lidzabwera kudzaukira Iguputo, ndipo anthu a ku Itiyopiya adzachita mantha kwambiri anthu akadzaphedwa ku Iguputo.

      Chuma cha Iguputo chidzalandidwa ndipo maziko ake adzagwetsedwa.+

  • Ezekieli 30:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Mumzinda wa Tahapanesi mudzagwa mdima masana ndikadzathyola magoli a Iguputo kumeneko.+ Mphamvu zimene amanyadira zidzatha.+ Mitambo idzamuphimba ndipo anthu amʼmatauni ake adzatengedwa kupita ku ukapolo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena