Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yeremiya 25:27, 28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 “Ndiyeno ukawauze kuti, ‘Yehova wa magulu ankhondo akumwamba, Mulungu wa Isiraeli wanena kuti: “Imwani ndipo muledzere, musanze ndi kugwa osadzukanso+ chifukwa cha lupanga limene ndikutumiza pakati panu.”’ 28 Ngati angakakane kulandira kapuyi mʼmanja mwako kuti amwe, ukawauze kuti, ‘Yehova wa magulu ankhondo akumwamba wanena kuti: “Mukuyenera kumwa basi.

  • Maliro 4:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Kondwa ndipo usangalale, iwe mwana wamkazi wa Edomu,+ amene ukukhala mʼdziko la Uzi.

      Koma iwenso kapu ya tsoka idzakupeza.+ Udzaledzera ndipo udzavula nʼkukhala maliseche.+

  • Obadiya 16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Mmene wamwera vinyo paphiri langa loyera,

      Ndi mmenenso mitundu ina yonse ya anthu izidzamwera mkwiyo wanga nthawi zonse.+

      Iwo adzamwa ndi kugugudiza mkwiyo wanga,

      Ndipo zidzakhala ngati sanakhalepo nʼkomwe.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena