Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 1:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Iye adzakhala ngati mtengo wodzalidwa mʼmbali mwa ngalande za madzi,

      Umene umabereka zipatso mʼnyengo yake,

      Umenenso masamba ake safota.

      Ndipo zonse zimene amachita zimamuyendera bwino.+

  • Salimo 92:12, 13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Koma olungama zinthu zidzawayendera bwino ngati mtengo wa kanjedza

      Ndipo adzakula kwambiri ngati mtengo wa mkungudza wa ku Lebanoni.+

      13 Iwo anadzalidwa mʼnyumba ya Yehova,

      Zinthu zikuwayendera bwino mʼmabwalo a Mulungu wathu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena