Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 126:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 126 Yehova atabwezeretsa anthu a ku Ziyoni kuchokera ku ukapolo,+

      Tinkangoona ngati tikulota.

  • Hoseya 6:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Komanso, inu anthu a ku Yuda, nthawi yoti mukololedwe yakhazikitsidwa.

      Ine ndidzasonkhanitsanso anthu anga amene anatengedwa kupita kudziko lina.”+

  • Amosi 9:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Ndidzasonkhanitsa ndi kubwezeretsa anthu anga Aisiraeli amene anatengedwa kupita ku ukapolo.+

      Iwo adzamanga mizinda imene ili yabwinja nʼkumakhalamo.+

      Adzalima minda ya mpesa nʼkumwa vinyo wake.+

      Adzalimanso minda nʼkudya zipatso zake.’+

  • Zefaniya 3:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Pa nthawiyo ndidzakubweretsani,

      Ndidzachita zimenezi pa nthawi imene ndidzakusonkhanitseni.

      Ndikadzabwezeretsa iwe ukuona, anthu a mtundu wako amene anatengedwa kupita ku ukapolo,+

      Ndidzachititsa kuti ukhale wotchuka* komanso uzitamandidwa,+ pakati pa anthu a mitundu yonse yapadziko lapansi,” watero Yehova.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena