Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 106:7, 8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Makolo athu ku Iguputo, sanayamikire* ntchito zanu zodabwitsa.

      Sanakumbukire chikondi chanu chokhulupirika chomwe ndi chochuluka,

      Koma anapanduka panyanja, pafupi ndi Nyanja Yofiira.+

       8 Koma Mulungu anawapulumutsa kuti dzina lake lilemekezedwe,+

      Kuti mphamvu zake zidziwike.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena