Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 66:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Ndidzaika chizindikiro pakati pawo ndipo ena mwa anthu amene adzapulumuke ndidzawatumiza ku mitundu ya anthu. Ndidzawatumiza kwa anthu aluso lokoka uta omwe ndi a ku Tarisi,+ ku Puli ndi ku Ludi.+ Ndidzawatumizanso kwa anthu a ku Tubala ndi ku Yavani+ komanso akuzilumba zakutali amene sanamvepo zokhudza ine kapena kuona ulemerero wanga. Iwo adzalengeza za ulemerero wanga pakati pa mitundu ya anthu.+

  • Ezekieli 27:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Iwe unkachita malonda ndi Yavani, Tubala+ ndi Meseki.+ Iwo ankakupatsa akapolo+ ndi zinthu zakopa kuti iwe uwapatse katundu wako.

  • Ezekieli 32:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Kumeneko nʼkumene kuli Meseki ndi Tubala+ limodzi ndi magulu a anthu awo onse amene ankawatsatira. Manda awo ali mozungulira mfumu yawo. Onsewa ndi anthu osadulidwa, anthu amene anabaidwa ndi lupanga chifukwa anachititsa kuti anthu amene akukhala mʼdziko la anthu amoyo azikhala mwamantha.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena