Yoweli 3:16 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 16 Yehova adzabangula kuchokera ku Ziyoni,Ndipo adzalankhula mokweza ali ku Yerusalemu. Kumwamba ndi dziko lapansi zidzagwedezeka.Koma Yehova adzakhala malo othawirako a anthu ake,+Malo achitetezo champhamvu kwa Aisiraeli. Nahumu 1:2 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 2 Yehova ndi Mulungu amene amafuna kuti anthu azidzipereka kwa iye yekha+ ndipo amabwezera adani ake.Yehova amabwezera adani ake ndipo ndi wokonzeka kusonyeza mkwiyo wake.+ Yehova amabwezera adani ake,Ndipo adani ake amawasungira mkwiyo. Zekariya 2:8 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 8 Atapatsidwa ulemerero, Mulungu wandituma kwa anthu a mitundu ina amene ankakulandani zinthu zanu,+ chifukwa Yehova wa magulu ankhondo akumwamba wanena kuti, ‘Amene akukukhudzani, akukhudza mwana wa diso langa.+
16 Yehova adzabangula kuchokera ku Ziyoni,Ndipo adzalankhula mokweza ali ku Yerusalemu. Kumwamba ndi dziko lapansi zidzagwedezeka.Koma Yehova adzakhala malo othawirako a anthu ake,+Malo achitetezo champhamvu kwa Aisiraeli.
2 Yehova ndi Mulungu amene amafuna kuti anthu azidzipereka kwa iye yekha+ ndipo amabwezera adani ake.Yehova amabwezera adani ake ndipo ndi wokonzeka kusonyeza mkwiyo wake.+ Yehova amabwezera adani ake,Ndipo adani ake amawasungira mkwiyo.
8 Atapatsidwa ulemerero, Mulungu wandituma kwa anthu a mitundu ina amene ankakulandani zinthu zanu,+ chifukwa Yehova wa magulu ankhondo akumwamba wanena kuti, ‘Amene akukukhudzani, akukhudza mwana wa diso langa.+