Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezekieli 1:3, 4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Yehova analankhula ndi Ezekieli,* mwana wa wansembe Buzi, pamene anali mʼdziko la Akasidi+ pafupi ndi mtsinje wa Kebara. Kumeneko mphamvu za Yehova zinayamba kugwira ntchito pa iye.*+

      4 Ndinaona mphepo yamkuntho+ ikuchokera kumpoto. Ndinaonanso mtambo waukulu komanso moto walawilawi*+ utazunguliridwa ndi kuwala. Pakati pa motowo panali chinachake chooneka ngati siliva wosakanikirana ndi golide.+

  • Ezekieli 3:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Choncho ndinanyamuka nʼkupita kuchigwako ndipo ndinaona kuti ulemerero wa Yehova uli kumeneko.+ Ulemerero umenewu unali wofanana ndi umene ndinauona pafupi ndi mtsinje wa Kebara+ ndipo ndinagwada nʼkuwerama mpaka nkhope yanga pansi.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena