Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yeremiya 52:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Kenako Akasidiwo anagwira mfumuyo nʼkupita nayo ku Ribila kwa mfumu ya Babulo mʼdziko la Hamati ndipo anaipatsa chigamulo.

  • Ezekieli 17:20, 21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Ndidzamuponyera ukonde wanga ndipo adzakodwa mu ukonde wanga wosakira.+ Ndiyeno ndidzamubweretsa ku Babulo nʼkumuweruza chifukwa chondichitira zinthu mosakhulupirika.+ 21 Asilikali ake onse amene anathawa adzaphedwa ndi lupanga ndipo amene adzapulumuke adzabalalikira kumbali zonse.*+ Zikadzatero mudzadziwa kuti ine Yehova ndi amene ndanena zimenezi.”’+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena