Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Esitere 3:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Kenako Hamani anauza Mfumu Ahasiwero kuti: “Pali mtundu wina wa anthu+ umene ukupezeka paliponse mʼzigawo zonse za ufumu wanu.+ Malamulo awo ndi osiyana ndi malamulo a anthu ena onse ndipo sakutsatira malamulo anu. Choncho ngati mungawasiye anthu amenewa, zinthu sizikuyenderani bwino mfumu.

  • Danieli 6:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Koma Danieli atangodziwa kuti lamulo limeneli lasainidwa, anapita kunyumba kwake. Mawindo a chipinda chake chamʼmwamba anali otsegula ndipo anayangʼana ku Yerusalemu.+ Katatu pa tsiku, iye ankagwada nʼkupemphera kwa Mulungu wake komanso kumutamanda, ngati mmene ankachitira nthawi zonse lamuloli lisanasainidwe.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena