Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Danieli 4:6, 7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Choncho ndinalamula kuti amuna onse anzeru a mʼBabulo awabweretse kwa ine kuti adzandimasulire malotowo.+

      7 Pa nthawi imeneyo ansembe ochita zamatsenga, anthu olankhula ndi mizimu, Akasidi* ndi okhulupirira nyenyezi+ anabwera kwa ine. Nditawafotokozera malotowo, sanathe kundiuza kumasulira kwake.+

  • Danieli 5:7, 8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Ndiye mfumuyo inaitana mofuula olankhula ndi mizimu, Akasidi* ndi okhulupirira nyenyezi.+ Mfumuyo inauza amuna anzeru a mʼBabulo amenewa kuti: “Aliyense amene angawerenge mawuwa nʼkundiuza kumasulira kwake, ndimuveka zovala zapepo ndi mkanda wagolide mʼkhosi+ ndipo akhala wolamulira wachitatu mu ufumuwu.”+

      8 Amuna onse anzeru anabwera kwa mfumu koma sanathe kuwerenga mawu amene analembedwawo kapena kuuza mfumu kumasulira kwake.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena