Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Danieli 8:23, 24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Kumapeto kwa ufumu wawo, zochita za anthu ochimwawo zikadzafika pachimake, mfumu yooneka mochititsa mantha ndiponso yomvetsa zinthu zovuta kumva idzayamba kulamulira. 24 Mphamvu za mfumuyo zidzachuluka, koma si iye amene adzachititse zimenezi. Idzawononga zinthu zambiri moti idzadabwitsa anthu. Chilichonse chimene mfumuyo izidzachita chizidzaiyendera bwino. Idzawononga anthu amphamvu ndi anthu oyera.+

  • Danieli 12:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Kenako ndinamva munthu amene anavala nsalu uja, amene anali pamwamba pa madzi amumtsinje akuyankha. Iye anakweza mʼmwamba dzanja lake lamanja ndi lamanzere nʼkulumbira pa Mulungu amene adzakhala ndi moyo mpaka kalekale,+ ndipo anati: “Padzadutsa nthawi imodzi yoikidwiratu, nthawi ziwiri zoikidwiratu ndi hafu ya nthawi yoikidwiratu.* Ndipo akadzangomaliza kuphwanyaphwanya mphamvu za anthu oyera,+ zinthu zonsezi zidzafika pamapeto.”

  • Chivumbulutso 13:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Chinaloledwa kumenyana ndi oyerawo nʼkuwagonjetsa.+ Chinapatsidwanso ulamuliro pa anthu a fuko lililonse, mtundu uliwonse, chilankhulo chilichonse ndi dziko lililonse.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena