Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Nehemiya 1:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 1 Awa ndi mawu a Nehemiya*+ mwana wa Hakaliya. Mʼmwezi wa Kisilevi,* mʼchaka cha 20, ine ndinali kunyumba ya mfumu yokhala ndi mpanda wolimba kwambiri ya ku Susani.*+

  • Esitere 2:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Ndiyeno anthu atalengeza mawu a mfumu ndiponso lamulo lake, komanso atasonkhanitsa atsikana ambiri kunyumba ya mfumu ku Susani* kuti Hegai aziwayangʼanira,+ Esitere nayenso anatengedwa kupita kunyumba ya mfumuyo kuti azikayangʼaniridwa ndi Hegai amene ankayangʼanira akazi.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena