Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 9:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Chifukwa anthuwo sanabwerere kwa Mulungu amene akuwamenya,

      Ndipo sanafunefune Yehova wa magulu ankhondo akumwamba.+

  • Yeremiya 5:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Inu Yehova, kodi si paja maso anu amayangʼana anthu amene ndi okhulupirika?+

      Mwawalanga koma sanamve kupweteka.*

      Ngakhale kuti munatsala pangʼono kuwawononga onse, iwo sanaphunzirepo kanthu.+

      Anaumitsa kwambiri nkhope zawo kuposa thanthwe,+

      Ndipo anakana kubwerera kwa inu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena