Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 45:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 45 Izi ndi zimene Yehova akunena kwa wodzozedwa wake, kwa Koresi,+

      Amene wamugwira dzanja lake lamanja+

      Kuti agonjetse mitundu ya anthu pamaso pake,+

      Kuti alande zida zankhondo za mafumu,*

      Kuti amutsegulire zitseko zokhala ziwiriziwiri,

      Kuti mageti adzakhale osatseka. Iye wamuuza kuti:

  • Yeremiya 51:28, 29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Sankhani* mitundu ya anthu kuti ichite naye nkhondo.

      Sankhani mafumu a ku Mediya,+ abwanamkubwa ake ndi achiwiri kwa olamulira awo onse

      Komanso mayiko onse amene iwo amawalamulira.

      29 Dziko lidzagwedezeka ndi kunjenjemera,

      Chifukwa Yehova adzachitira Babulo zimene akuganiza

      Kuti dziko la Babulo likhale chinthu chochititsa mantha, lopanda munthu wokhalamo.+

  • Danieli 5:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 PERESI, ufumu wanu wagawidwa ndipo waperekedwa kwa Amedi ndi Aperisiya.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena