Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 5:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Koma Farao anati: “Yehova ndi ndani+ kuti ndimvere mawu ake nʼkulola Aisiraeli kuti apite?+ Ine sindikumudziwa Yehova ngakhale pangʼono ndipo sindilola kuti Aisiraeli apite.”+

  • 2 Mbiri 32:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Musalole kuti Hezekiya akupusitseni kapena kukusocheretsani chonchi.+ Musamukhulupirire, chifukwa palibe mulungu wa ufumu uliwonse kapena wa mtundu uliwonse amene anatha kupulumutsa anthu ake mʼmanja mwanga ndiponso mʼmanja mwa makolo anga akale. Ndiye mukuganiza kuti Mulungu wanu angakupulumutseni mʼmanja mwanga?’”+

  • Yesaya 36:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Choncho Rabisake anawauza kuti: “Mukauze Hezekiya kuti, ‘Mfumu yaikulu, mfumu ya Asuri yanena kuti: “Kodi ukudalira chiyani?+

  • Yesaya 36:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Ndi mulungu uti pa milungu yonse ya mayiko amenewa, amene wapulumutsa dziko lake mʼmanja mwanga, kuti Yehova athe kupulumutsa Yerusalemu mʼmanja mwanga?”’”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena