-
2 Mbiri 32:15Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
15 Musalole kuti Hezekiya akupusitseni kapena kukusocheretsani chonchi.+ Musamukhulupirire, chifukwa palibe mulungu wa ufumu uliwonse kapena wa mtundu uliwonse amene anatha kupulumutsa anthu ake mʼmanja mwanga ndiponso mʼmanja mwa makolo anga akale. Ndiye mukuganiza kuti Mulungu wanu angakupulumutseni mʼmanja mwanga?’”+
-