Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yeremiya 22:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Ndidzakutumizira anthu oti akuwononge,

      Aliyense adzabwera ndi zida zake.+

      Iwo adzadula mitengo yako ya mkungudza yabwino kwambiri

      Ndipo adzaigwetsera pamoto.+

  • Yeremiya 46:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Uwu ndi uthenga wokhudza Iguputo+ wonena za gulu la asilikali a Farao Neko,+ mfumu ya Iguputo, amene anagonjetsedwa ndi Nebukadinezara* mfumu ya Babulo ku Karikemisi, mʼmbali mwa mtsinje wa Firate. Anagonjetsedwa ndi mfumu imeneyi mʼchaka cha 4 cha ulamuliro wa Yehoyakimu+ mwana wa Yosiya, mfumu ya Yuda. Uthengawo unali wakuti:

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena