Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 114:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 114 Isiraeli atatuluka mu Iguputo,+

      Nyumba ya Yakobo itatuluka pakati pa anthu olankhula chilankhulo chachilendo,

  • Salimo 114:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Mapiri anadumphadumpha ngati nkhosa zamphongo,+

      Zitunda zinadumphadumpha ngati ana a nkhosa.

  • Nahumu 1:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Mapiri akuluakulu amagwedezeka chifukwa cha iye.

      Ndipo mapiri angʼonoangʼono amasungunuka.+

      Dziko lapansi lidzanjenjemera chifukwa cha nkhope yake

      Pamodzi ndi nthaka komanso zinthu zonse zokhala mʼdzikomo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena