Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezekieli 28:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 “Iwe mwana wa munthu, yangʼana ku Sidoni+ ndipo ulosere zoipa zimene zidzamuchitikire.

  • Yoweli 3:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Komanso kodi ndakulakwira chiyani

      Iwe Turo ndi Sidoni ndiponso nonse amʼchigawo cha Filisitiya?

      Kodi mukundichitira zimenezi pondibwezera zimene ndinachita?

      Ngati mukundibwezera,

      Ine ndidzakubwezerani mwamsanga ndiponso mofulumira zimene mwandichitirazo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena