4 Komanso kodi ndakulakwira chiyani
Iwe Turo ndi Sidoni ndiponso nonse amʼchigawo cha Filisitiya?
Kodi mukundichitira zimenezi pondibwezera zimene ndinachita?
Ngati mukundibwezera,
Ine ndidzakubwezerani mwamsanga ndiponso mofulumira zimene mwandichitirazo.+