-
Ezekieli 34:8Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
8 ‘“Pali ine Mulungu wamoyo,” akutero Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, “nkhosa zanga zagwidwa ndipo zakhala chakudya cha zilombo zonse zakutchire chifukwa panalibe mʼbusa ndipo abusa anga sanazifunefune. Koma ankangodzidyetsa okha, osadyetsa nkhosa zanga.”’
-