-
Ezekieli 34:6Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
6 Nkhosa zanga zinasochera mʼmapiri onse ndi mʼzitunda zonse zitalizitali. Nkhosa zanga zinabalalika padziko lonse lapansi ndipo panalibe amene ankazifufuza kapena kuziyangʼanayangʼana.
-