Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 56:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Inu mukudziwa bwino za kuthawathawa kwanga.+

      Sungani misozi yanga mʼthumba lanu lachikopa.+

      Kodi misozi yanga sinalembedwe mʼbuku lanu?+

  • Salimo 69:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Mayina awo afufutidwe mʼbuku la anthu amoyo,*+

      Ndipo iwo asalembedwe mʼbuku limene muli mayina a anthu olungama.+

  • Yesaya 26:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Inu Yehova, pamene tikutsatira njira ya ziweruzo zanu,

      Chiyembekezo chathu chili pa inu.

      Tikulakalaka dzina lanu komanso zimene dzinalo limaimira.*

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena