Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Luka 4:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Kenako anapita ku Nazareti+ kumene anakulira. Mogwirizana ndi chizolowezi chake pa tsiku la Sabata, analowa mʼsunagoge+ nʼkuimirira kuti awerenge Malemba.

  • Machitidwe 13:13, 14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Kenako Paulo ndi anzakewo, anayamba ulendo wa panyanja kuchoka ku Pafo, ndipo anakafika ku Pega, ku Pamfuliya. Koma Yohane+ anawasiya nʼkubwerera ku Yerusalemu.+ 14 Atachoka ku Pega anakafika ku Antiokeya wa ku Pisidiya. Kumeneko analowa mʼsunagoge+ tsiku la Sabata nʼkukhala pansi.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena