Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Maliko 7:20-22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Iye ananenanso kuti: “Chotuluka mʼthupi la munthu nʼchimene chimaipitsa munthu.+ 21 Chifukwa mumtima mwa anthu+ mumatuluka maganizo oipa ngati: zachiwerewere,* zakuba, zopha anthu, 22 zachigololo, dyera, kuchita zoipa, chinyengo, khalidwe lopanda manyazi,* diso la kaduka, mawu onyoza, kudzikweza ndiponso kuchita zinthu mopanda nzeru.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena