Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Miyambo 19:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Amene amakomera mtima munthu wonyozeka akukongoza Yehova,+

      Ndipo adzamʼbwezera* zimene anachitazo.+

  • Mateyu 10:42
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 42 Aliyense wopatsa mmodzi wa tiana iti ngakhale madzi ozizira okha mʼkapu kuti amwe chifukwa ndi wophunzira wanga, ndithu ndikukuuzani, ameneyo mphoto yake sidzatayika ngakhale pangʼono.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena