Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 3:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Nkhwangwa yaikidwa kale pamizu yamitengo. Choncho mtengo uliwonse wosabereka zipatso zabwino udulidwa nʼkuponyedwa pamoto.+

  • Luka 13:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Kenako anayamba kufotokoza fanizo ili: “Munthu wina anali ndi mtengo wamkuyu mʼmunda wake wa mpesa, ndipo anapita kukafuna chipatso mumtengowo, koma sanapezemo chilichonse.+

  • Luka 13:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Ukadzabereka zipatso mʼtsogolo, zidzakhala bwino, koma ngati sudzabereka mudzaudule.’”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena