Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 8:3, 4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Choncho Yesu anatambasula dzanja lake nʼkumukhudza ndipo ananena kuti: “Inde ndikufuna. Khala woyera.”+ Nthawi yomweyo khate lakelo linatha.+ 4 Ndiyeno Yesu anamuuza kuti: “Samala, usauze aliyense zimenezi,+ koma upite ukadzionetse kwa wansembe+ ndipo ukapereke mphatso imene Mose analamula,+ kuti ikhale umboni kwa iwo.”

  • Maliko 3:11, 12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Ngakhalenso mizimu yonyansa,+ inkati ikamuona, inkadzigwetsa pansi pamaso pake nʼkufuula kuti: “Inu ndinu Mwana wa Mulungu.”+ 12 Koma mobwerezabwereza iye anailamula mwamphamvu kuti isamuulule.+

  • Maliko 7:35, 36
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 35 Atatero, makutu ake anatseguka+ ndipo vuto lake losalankhulalo linatheratu, moti anayamba kulankhula bwinobwino. 36 Ndiyeno anawalamula kuti asauze aliyense zimene zinachitikazo.+ Koma ankati akawaletsa mwamphamvu kuti asauze aliyense, mʼpamenenso iwo ankazifalitsa kwambiri.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena