Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Maliko 3:31-35
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 Tsopano panafika mayi ake ndi azichimwene ake+ ndipo anaima panja nʼkutuma munthu kuti akamuitane.+ 32 Gulu la anthu linakhala momuzungulira ndipo anthuwo anamuuza kuti: “Mayi anu ndi azichimwene anu ali panjapa akukufunani.”+ 33 Koma iye anawayankha kuti: “Kodi mayi anga ndi azichimwene anga ndi ndani?” 34 Kenako anayangʼana onse amene anakhala pansi momuzungulira aja nʼkunena kuti: “Onani! Mayi anga ndi azichimwene anga ndi awa.+ 35 Aliyense amene amachita zimene Mulungu amafuna, ameneyo ndi mchimwene wanga, mchemwali wanga ndi mayi anga.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena