Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Maliko 4:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Choncho mbewu zimene zimagwera mʼmbali mwa msewu ndi mawu amene afesedwa mwa anthu amene amati akangomva mawuwo, Satana amabwera+ nʼkudzachotsa mawu amene afesedwa mwa iwo.+

  • Luka 8:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Zogwera mʼmbali mwa msewuzo ndi anthu amene amamva mawuwo. Kenako Mdyerekezi amabwera nʼkudzachotsa mawuwo mʼmitima yawo kuti asakhulupirire ndiponso kupulumuka.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena