Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 23:15, 16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Tsoka kwa inu alembi ndi Afarisi, anthu achinyengo inu!+ Chifukwa mumawoloka nyanja komanso kuyenda mitunda italiitali kuti mukatembenuze munthu mmodzi. Koma akatembenuka mumamupangitsa kuti akhale woyenera kuponyedwa mʼGehena* kuposa inuyo.

      16 Tsoka kwa inu atsogoleri akhungu,+ amene mumati, ‘Ngati munthu watchula kachisi polumbira, palibe kanthu, koma ngati munthu watchula golide wa mʼkachisi, akuyenera kusunga lumbiro lake.’+

  • Luka 6:39
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 39 Kenako anawauzanso fanizo lakuti: “Munthu wosaona sangatsogolere wosaona mnzake, angatero ngati? Ngati angatero onse awiri angagwere mʼdzenje, si choncho?+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena