Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Maliko 7:25-30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Nthawi yomweyo, mayi wina amene mwana wake wamkazi anagwidwa ndi mzimu wonyansa anamva za iye ndipo anabwera nʼkudzagwada pamapazi ake.+ 26 Mayiyu anali Mgiriki, wa Chisurofoinike. Iye anapempha Yesu mobwerezabwereza kuti atulutse chiwanda mwa mwana wakeyo. 27 Koma Yesu anauza mayiyo kuti: “Choyamba, zimafunika kuti ana akhute kaye, chifukwa si bwino kutenga chakudya cha ana nʼkuponyera tiagalu.”+ 28 Koma mayiyo anamuyankha kuti: “Inde mbuyanga, komatu tiagalu timadya nyenyeswa za anawo pansi pa tebulo.” 29 Yesu atamva zimenezo anauza mayiyo kuti: “Chifukwa chakuti wanena zimenezi, pita, chiwandacho chatuluka mwa mwana wakoyo.”+ 30 Choncho anapita kunyumba kwake ndipo anakapeza mwanayo atagona pabedi chiwandacho chitatuluka.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena