Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Levitiko 19:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Usamadane ndi mʼbale wako mumtima mwako,+ koma uzimudzudzula+ kuti iwenso usakhale wochimwa ngati iyeyo.

  • Miyambo 25:8, 9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Usamafulumire kupititsa mlandu kukhoti,

      Chifukwa udzachita chiyani mnzako akadzapereka umboni wosonyeza kuti iweyo ndi wolakwa?+

       9 Thetsa nkhaniyo pokambirana ndi mnzakoyo,+

      Koma usaulule nkhani zachinsinsi zimene unauzidwa,*+

  • Luka 17:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Samalani ndithu. Ngati mʼbale wako wachita tchimo umudzudzule+ ndipo akalapa umukhululukire.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena