Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 53:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Chifukwa cha kuvutika kwake, iye adzaona zabwino ndipo adzakhutira.

      Chifukwa cha zimene mtumiki wanga wolungama akudziwa,+

      Adzachititsa kuti anthu ambiri azionedwa olungama,+

      Ndipo adzanyamula zolakwa zawo.+

  • Maliko 10:45
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 45 Chifukwa ngakhale Mwana wa munthu sanabwere kudzatumikiridwa koma kudzatumikira+ ndi kudzapereka moyo wake dipo* kuti awombole anthu ambiri.”+

  • 1 Timoteyo 2:5, 6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Chifukwa pali Mulungu mmodzi+ ndiponso mkhalapakati mmodzi+ pakati pa Mulungu ndi anthu.+ Mkhalapakatiyu ndi Khristu Yesu,+ munthu 6 amene anadzipereka kuti akhale dipo* la anthu onse lokwanira ndendende.+ Zimenezi ndi zimene zidzachitiridwe umboni pa nthawi yake.

  • Tito 2:13, 14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 pamene tikuyembekezera zinthu zosangalatsa+ ndiponso kuonekera kwaulemerero kwa Mulungu wamkulu komanso kwa Mpulumutsi wathu, Yesu Khristu, 14 amene anadzipereka mʼmalo mwa ife+ kuti atilanditse*+ ku moyo wochita zinthu zosamvera malamulo za mtundu uliwonse ndiponso kuti atiyeretse, kuti tikhale anthu ake apadera, odzipereka pa ntchito zabwino.+

  • Aheberi 9:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 nayenso Khristu anaperekedwa nsembe kamodzi kokha kuti anyamule machimo a anthu ambiri.+ Nthawi yachiwiri imene adzaonekere sadzaonekera nʼcholinga chochotsa uchimo. Ndipo amene adzamuone ndi anthu amene akumuyembekezera ndi mtima wonse kuti awapulumutse.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena