Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Maliko 11:4-6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Choncho iwo ananyamuka ndipo anapezadi bulu wamphongo atamumangirira pakhomo, mʼmphepete mwa msewu waungʼono. Ndipo iwo anamasula buluyo.+ 5 Koma ena mwa anthu amene anali ataimirira chapomwepo anawafunsa kuti: “Cholinga chanu nʼchiyani pomasula buluyu?” 6 Iwo anawauza zimene Yesu ananena ndipo anawalola kuti apite.

  • Luka 19:32-35
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 32 Choncho anthu amene anatumidwawo ananyamuka ndipo anakamupezadi mmene iye anawauzira.+ 33 Koma pamene ankamasula buluyo, eniake anawafunsa kuti: “Nʼchifukwa chiyani mukumasula buluyu?” 34 Iwo anayankha kuti: “Ambuye akumufuna.” 35 Pamenepo iwo anamutenga nʼkupita naye kwa Yesu. Kenako iwo anaponya malaya awo akunja pabuluyo ndipo Yesu anakwerapo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena