Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Maliko 11:15, 16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Tsopano iwo anafika ku Yerusalemu. Kumeneko analowa mʼkachisi nʼkuyamba kuthamangitsa anthu amene ankagulitsa ndi kugula zinthu mʼkachisimo, ndipo anagubuduza matebulo a anthu amene ankasintha ndalama komanso mabenchi a anthu amene ankagulitsa nkhunda.+ 16 Iye sanalole aliyense kuti adutse mʼkachisimo atanyamula katundu.

  • Luka 19:45
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 45 Ndiyeno analowa mʼkachisi nʼkuyamba kuthamangitsa anthu amene ankagulitsamo zinthu+

  • Yohane 2:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Choncho anapanga chikwapu chazingwe nʼkuthamangitsa onse amene anali ndi nkhosa komanso ngʼombe mʼkachisimo. Anakhuthula makobidi a anthu osintha ndalama nʼkugubuduza matebulo awo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena