Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Luka 20:37, 38
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 37 Koma zakuti akufa amaukitsidwa ngakhalenso Mose anafotokoza munkhani ya chitsamba cha minga, pamene ananena kuti Yehova* ndi ‘Mulungu wa Abulahamu, Mulungu wa Isaki ndi Mulungu wa Yakobo.’+ 38 Iye ndi Mulungu wa anthu amoyo, osati akufa, chifukwa kwa iye* onsewa ndi amoyo.”+

  • Aroma 4:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 (Zimenezi nʼzogwirizana ndi zimene Malemba amanena kuti: “Ndakusankha kuti ukhale bambo wa mitundu yambiri.”)+ Izi zinali choncho pamaso pa Mulungu amene Abulahamu ankamukhulupirira, yemwenso amaukitsa akufa ndipo amanena za zinthu zimene palibe ngati kuti zilipo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena