Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Luka 4:9-12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Kenako anapita naye ku Yerusalemu ndipo anamukweza pamwamba pa khoma la mpanda wa kachisi* nʼkumuuza kuti: “Ngati ndinu mwana wa Mulungu, mudziponye pansi kuchokera pano.+ 10 Paja Malemba amati, ‘Iye adzalamula angelo ake zokhudza inu, kuti akutetezeni,’ 11 ndipo ‘Adzakunyamulani mʼmanja mwawo, kuti phazi lanu lisawombe mwala.’”+ 12 Poyankha Yesu anamuuza kuti: “Malemba amati, ‘Yehova* Mulungu wanu musamamuyese.’”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena