Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 12:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Mʼmwezi woyamba, tsiku la 14 la mwezi umenewo, madzulo muzidzadya mikate yopanda zofufumitsa, mpaka kukafika madzulo a tsiku la 21 mwezi womwewo.+

  • Ekisodo 23:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Muzichita Chikondwerero cha Mikate Yopanda Zofufumitsa.+ Muzidya mikate yopanda zofufumitsa masiku 7 pa nthawi imene inaikidwa mʼmwezi wa Abibu*+ mogwirizana ndi zimene ndinakulamulani, chifukwa munatuluka mu Iguputo mʼmwezi umenewu. Ndipo palibe amene ayenera kuonekera kwa ine chimanjamanja.+

  • Luka 22:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Tsopano Chikondwerero cha Mikate Yopanda Zofufumitsa, chimene chinkadziwikanso kuti Pasika,+ chinali chitayandikira.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena