Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Maliko 14:55-59
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 55 Ndiyeno ansembe aakulu ndi Khoti lonse Lalikulu la Ayuda ankafunafuna umboni kuti anamizire Yesu mlandu nʼcholinga choti amuphe, koma sanaupeze.+ 56 Anthu ambiri ankapereka umboni wabodza kuti amunamizire mlandu,+ koma maumboni awowo ankatsutsana. 57 Komanso, anthu ena ankaimirira nʼkumapereka umboni womunamizira kuti: 58 “Ife tinamva iyeyu akunena kuti, ‘Ine ndidzagwetsa kachisi uyu amene anamangidwa ndi manja ndipo mʼmasiku atatu okha ndidzamanga wina osati womangidwa ndi manja.’”+ 59 Komabe ngakhale pa mfundo zimenezi, umboni wawo sunali wogwirizana.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena