Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Maliko 14:62
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 62 Ndiyeno Yesu ananena kuti: “Inde ndinedi, ndipo mudzaona Mwana wa munthu+ atakhala kudzanja lamanja+ lamphamvu. Mudzamuonanso akubwera ndi mitambo yakumwamba.”+

  • Yohane 5:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Pa chifukwa chimenechi Ayudawo anayamba kufunafuna njira yoti amuphere, chifukwa kuwonjezera pa kuphwanya Sabata, ankanenanso kuti Mulungu ndi Atate wake,+ kudziyesa wofanana ndi Mulungu.+

  • Yohane 10:36
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 36 kodi inu mukundiuza ine amene Atate anandiyeretsa nʼkunditumiza mʼdziko kuti, ‘Ukunyoza Mulungu,’ chifukwa ndanena kuti, ‘Ndine Mwana wa Mulunguʼ?+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena